NTHANO YA Koma kwa kanthawi kochepa Yohane anayamba Child helpline ndi kabungwe
kufunsa Bwalya nkhani yakufuna kugona naye kamene mwachidule kamathandizira
BWALYA m'malo amodzi chinthu chimene Bwalya anakana. mwachinsinsi ana ndi iwo
achichepele pa zinthu zamene
Khalidwe lokhala olumikizidwa ndi zoulusa Mwakubwezela, Yohane anatumiza zingavute pa moyo wawo.
or kapena kunena kuti pa neti lakhala mbali zinthunzinthunzi za Bwalya alimaliseche pa neti.
yayikulu ya miyoyo yathu. Pali zinthu zambiri Lifeline / Childline Zambia ndi ka
zomwe tingachite pa zoulutsira or kapena Bwalya analemba ma uthenga kumupempha bungwe kapadera kamene kama chita
kunena kuti pa neti,zinthu monga kusewera Yahone kuti achose zinthunzithunzi koma Yohane zauphungu, chisogozo ndi kutumiza pa ma lamya
masewera akanema olo kepena kungo cheza ndi anangosula ma uthenga ameneo? kwa azibambo,azimai,anyamata ndi atsikana amene
abwenzi,koma ndi chofunikila kuti tonse tikhale akukumana nazo zobvuta zosiyanasiyana.
otetezedwa bwino pamene tichita zimenezi. Kodi Ndi chiyani chemene Bwalya angachite?
Masomphenya a kabungwe aka ndi kukhala
Walya ndi mtsikana amene Kodi mudziwa kuti kuli mau ambiri amene ana osachitilana zaupandu mumadera amene
ali ndi zaka 14 kapena khumi amasiwenzetsa pa kunena za ziwalo zapathupi tikhalilaulele.a mdziko lathu la Zambia ndipo tigwapo
ndi zinayi amene akhala ku matero, mu zobisika? Ena mau moonjezera ndi: pa kuteteza,kupatsa mphamvu ndi kuthandizira
Lusaka. mabungwe maka maka ya adzimai ndi ana m'madera
kunena paza akuti ku kuboma kapena Malo athu, kukhala umoyo wabwino wopanda chiwawa
Mtsikana ameneyu akhala ali kuchita Kumbuyo Thako olemekezeka cha pa jenda ,kuthandauza kuti ukhala umoyo
chisumbali ndi Yohane amene ali ndi zaka wotetezedwa ku cikhalidwe cosankhana paza ufulu
makhumi awiri ndi zisanu ndi cimodzi 26 ku danana ku dudu ku John wa cibadwidwe.
ndipo achokela ku ka mwala,Mu Lusaka.
Malo onzuna ku ujeni ku umunthu Ali ndi manambala othandizira awiri: Lifeline 933 ndi
ChisumbalI chimenechi chakhala pafupifupi Childline 116, manambala awa ndi ulele kopanda
chaka chimozi. ?? kulipila ndipo asebenza usana ndi usiku pa ma
netweki onse mu Zambia. 116 ninambala yamene
Masiku ochepa akumbuyo uku Yohane ? ina patsidwa ku ana achichepele chabe,koma 933
anafunsa Bwalya kuti amtumizile zinthunzi ninambala ya ana ndi akulu.
nthuzi zake zamaliseche olo kapena kunena Bwalya anada nkhawa kweni- kweni ndipo
kuti zopanda zovala. Ndipo pachiyambi pake anafunitsitsa thandizo kuti akambeko ndi munthu Ndi kabungwe kokhulupililika kuthandizila
pa nkhaniyi Bwalya anadodoma kunena kuti wina yemwe angalabadire ndi kukhulupilira. mabvuto amene apezeka pakati ka
sanafune kuchita zimenezi koma pambuyo azimai,azibambo,anyamata,atsikana,ana achichepele
pake anadzijambula zinthunzi nthunzi Ndipo Bwalya anakumbukila zimene anauzidwa ndi wina aliyense mu ziko la Zambia amene akumana
alimaliseche namtumizira Yohane chifukwa ku sukulu natuma lamya ku child helpline, Lifeline / ndi mabvuto a kuzunzidwa, kugonana ndi mabvuto
anayopa kuti chisumbali chao chingathe. Childline Zambia pakutumila pa nambala iyi 116. a m’maganizo ndikufuna wina angakambe zimene
zifunika munthu ali ndi dzitu lomvetsa madandaulowa,
kopanda kuwagamula mlandu wosaweluzidwa
Aphungu odziwa zitundu zosiyanasiyana ali
ophunzitsidwa ndipo ndiakaswili pa kuthandiza
zofunikila ana, achichepele Ndi akulu omwe
pakuvetsela, kutumiza kwamene iwo akhoza kupeza
thandizo,ku police,ku chipatala kulingana ndivuto
angapezeke nalo.
Pambuyo pakuimba lamya pa nambala ya 116 Kodi hotline ndi ciani? Ndipo Phungu analangiza Bwalya mokhalira celu
Bwalya analankhulitsana ndimphungu amene pa mphamvu ya internet pamene akuceza ndi anthu
ndikaswili pa kumvetsela,kulankhulitsana Nambala ya thandizo ndi nambala yoikidwa potsatira. Izi zinsinsi ndiye:
ndi ana ndi kuwathandiza. Anafotokozera kuti yithandizile kupanga dziko lapansi kukhala
mphungu meneyu zonse zomwe zinachitika lotetezedwa kwa munthu wina aliyense. Unganizira amene ukuceza naye kuti ndan.
ndi mumene anali kumvelera pa nkhaniyi. Ngati mwatsoka inu muona zithunzi thunzi olo
ma filimu ya kugonana ya munthu amene inu Osaulusa za umoyo wako pa neti ngakhale fungulo
Wopeleka uphungu waku Lifeline / Childline muganizila ali ndi zaka zochepa pa 18( khumi ndi zachinsinsi.
Zambia anamvetsera ndi kuuza Bwalya zisanu ndi zitatu),inu mufunika kutuma lamya ku
kuti zimene zinacitika sizinali bwino ndipo nambala yathandizo. Aja akaswili pa nkhani zofufuza Unganiza usanatume kalikonse pa net.
anamuthokoza polimba mtima kuzazena azayetsetsa kwambili kuchosa zinthunzithunzi ndi
nkhaniyi. Izi zinamumvetsako bwino Bwalya. mafilimu amaliseche ndikugonana pa neti. Uganizira ena, kuwapatsa ulemu oyenera ndiponso
osatuma zithu zosaloledwa koma cabe maunthenga
Mphunguyu, analangiza bwalya pomupatsa Kodi zipata za nambala yathandizo nichani?
uphungu ndi malangizo, komanso cymene oyenelera. Osatuma zithunzi za ena kopanda
angacite pazazithunzizo zimene zinali pa Ichi ndiye chisanzo chaziko lina kuthandizila ziko cilolezo cawo.
mphepo ya internet. Anamuuzanso za hotline linanso limene lilibe nambala yathandizo. Inu mukhoza
(nambala ndi nchito yace). kunena ku zipata zonenelako munga muchitila Kuti adziwe zambiri, Bwalya anapatsidwa njira imene
kunambala yathandizo. angathe kugwiritsa nchito iyi ndi;
Ndi thandizo lochokela kwa mphungu
Bwalya anakwanisa kuchita lipoti pa zipata Mwaichi ngati muona mwangozi zinthunzithunzi Lifeline / Childline Zambia
zopangilapo ma lipoti. kapena ma filimu akugonana gonana ya munthu https://clzambia.org/
amene inu muganizila kuti ali ndizaka zofika pa 18
Pambuyo pace anamvako bwino pamene ,mukhoza kuchita chilungamo ndi mo bisa zina lanu StopIt
anatsimikiza kuti pali wina azacitapo kanthu nenani apa: www.stopit.ac.zm/resources
pa nkhani yace ya zithunzi zace zosayenera
zija zinali pa phempo. StopIt ZICTA
www.stopit.ac.zm https://www.zicta.zm/
Ngati mukhala ndivuto ndi neti pa nthawi imene inu Asadule lamya, phungu, anamfunsa Bwalya
mufuna kuchita lipoti koma mukali kufunisisa kuti ngati kungakhale kotheka kuti azilankhuzana.
mukambisane ndi wina pa kufuna thandizo,inu tumani Phunguyu adaonga Bwalya powadalira kuti
lamya ku Lifeline / Childline Zambia pa 116. amthandize ndiponso anamuuza kuti auze
anzake onse angafune thandizo kuti azikhala
omasuka kutuma nthawi ina iliyonse. Pothera
pene- pene Bwalya anauzidwa kuti akhale
omasuka nthawi zones.